06/07/2025
Congratulations to you beans Raphael Sitima
Today you are responsible man sangalani kuti mwalowa m'banja
Langizo banja ndi ulendo ndipo mukumana ndizambiri.Zabwino,zowawa, myozo,kusanvana,kusphana zichewa.
Ndilipo mwana padali nkuluwina aniakonda nyimbo izi polanga ukwati
1.ukugugu ukugugu wadya nsima ya mwana osasamba mmanja
2.kapilire kunkaiweko kapilire kunkaiweko
Kumeneko kuli ana eee kumeneko kuli ana eee osasamba eee amanthongo eeeee kapilire kunkaiweko
Mmagsnizo mwanga ndinkaona ngati anawo ndi
eni eni amoyo koma ayi ndithu adali mavuto am'banja
3.nankholowa watamba tamba kusaukira utundu nyimbo zomwe inenso ndikufuna kuti munvemo malangizowo sanakusankhireni
Kamukondeni moyo wanuonse nyimbo ikhale ya Lucioas Banda ft.san b Kennedy