04/05/2026
NDE KULI UYU AMATI Morton Baghaya KUMAPANGA BACK ZINTHU ZOPUSA😪
ZOTI MUZIYIPISA DZINA LA MULUNGU MMM MUZINGOCHIMWIRAPO APA POMWE PALAKWIKA PLZ DZUDZULAN OSABAKIRA USILU AYI, UYU MIRACLE VIC CHING UYU PANO KUNENADI ZAOONA PA GOSPEL ANATCHOKAPO CHIFUKWA NYIMBO ZAKE NDI KHALIDWE LOMWE AKULIONESA ZOSIYANA KUTALI CHIFUKWA MAU AKUTI
1 Timoteyo 2:9
Ndikufunanso kuti amayi azivala mwaulemu, modzilemekeza ndi moyenera. Adzikongoletse koma osati ndi tsitsi loluka mowonjeza muyeso kapena zokongoletsa zagolide kapena mikanda yamtengowapatali kapena ndi zovala zamtengowapatali.
1 Timoteyo 2:10
Koma adzikongoletse ndi ntchito zabwino zoyenera mayi wopembedza Mulungu.
NDE ALIYESE AMENE AKUBAKIRA ZINTHU NGATI IZI IYESO AMAKHALA MUZOMWEZO
ZIKOMO
MUUZENI UYU MULUNGU SI DZINA LOLISEWERESA
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏