Autice Mdzuma the poet

Autice Mdzuma the poet Poet and Chinese student

mdalitso wina ukukusemphano chifukwa cha aja mudawakwiira aja, tawakhululukiran muone chikondi cha mulungu leroHappy Sun...
03/05/2026

mdalitso wina ukukusemphano chifukwa cha aja mudawakwiira aja, tawakhululukiran muone chikondi cha mulungu lero

Happy Sunday🥳

nanga momwe wavutira Malawi basi wina azidulitsa phon nanga munda🤣
02/05/2026

nanga momwe wavutira Malawi basi wina azidulitsa phon nanga munda🤣

02/05/2026

kutengeka, kufuna kufanana level ndi a nebor zotsaitira zake ndi zimenezo 🤣🤣

Album yomwe Mlakatuli Raphael Sitima akutulutsa mawa, only Autice mdzuma the poet  featured one of his poem   . tiyeni t...
02/05/2026

Album yomwe Mlakatuli Raphael Sitima akutulutsa mawa, only Autice mdzuma the poet featured one of his poem . tiyeni tikumane ku lilongwe CCAP hall mawa laliwisili tikayapatse motsooo🥳🥳🥳🥳

01/05/2026

Nthawi ya moyo zochitika ndizambiri.
ngati wakuswani mtima ndiye kuti muli mu nthawi ya moyo. open new chapter 😎

The staaaaaaaageeee master Raphael sitima ali ndi show kuseli kwa mawa uku, kulalikira walalikira koma tsiku ili ndiloma...
01/05/2026

The staaaaaaaageeee master Raphael sitima ali ndi show kuseli kwa mawa uku, kulalikira walalikira koma tsiku ili ndilomaliza, tiyeeeeenni tonse tikakumane ku lilongwe CCAP hall kodi inu zabwino ayiiiiii???🥳🥳🥳

LISTEN TO MY STORY ON LABOURS DAY 🙏🙏🙏🙏🙏🙏😭😭I was born into a poor family of eight children in a rural village, life was n...
01/05/2026

LISTEN TO MY STORY ON LABOURS DAY 🙏🙏🙏🙏🙏🙏😭😭

I was born into a poor family of eight children in a rural village, life was never easy. We could not always afford proper clothes or even a good meal, but the desire to learn never left me.

I started primary school at the age of 8, later went on to Dowa Secondary School, and by God’s grace, I passed my MSCE becoming the only person in my entire village to achieve it. That moment changed everything.

I continued my journey at Kasungu Teachers Training College, and in 2018, I began my career as a professional teacher. But I didn’t stop there.

In 2024, I took another bold step and enrolled at MUST to study a Bachelor of Arts in Languages and Communication, specializing in Chinese and English.

Looking back, I see not just struggle, but strength. Not just lack, but determination. And above all, God’s hand guiding me every step of the way.

I thank God for this journey 🙏🙏🙏

Happy labours day

30/04/2026

from inbox
"I am 30yrs man, am looking for FAIRY used woman of about 25-28 yrs"

Alamu anu akuchimuna abwera ndi mwana kwanu, akukuuzani kuti musamuletse amalira. ladies let's goo🤣
30/04/2026

Alamu anu akuchimuna abwera ndi mwana kwanu, akukuuzani kuti musamuletse amalira. ladies let's goo🤣

ena simundidzwa koma mukachita search pa Google ikupatsani information yonse, osaiwala tili ndi album launch ya Raphael ...
30/04/2026

ena simundidzwa koma mukachita search pa Google ikupatsani information yonse, osaiwala tili ndi album launch ya Raphael sitima ku lilongwe pa 3 May. lets cast our last tickets now.

29/04/2026

palia tickets awiri a show ya Raphael ndipereka kwa amene comment yake sikhala ndi like
tchulani ubwino umodz okhala single😂

malinga mkudula kwa fuel, ku Dowa stikupanga nawo zibwana😂
29/04/2026

malinga mkudula kwa fuel, ku Dowa stikupanga nawo zibwana😂

Address

Lilongwe

Telephone

+265990492726

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Autice Mdzuma the poet posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Establishment

Send a message to Autice Mdzuma the poet:

Share