05/04/2026
Anthu a ku Burkina Faso ayamba kumutchula Ibrahim Traore kuti President wamuyayaππ»
Izi zikuza pamene azungu amafuna alowere pa ganizo lomwe Ibrahim Traore wayankhura lokhunza kuipa kwa Democracy
Azunguwo anayamba kutuma anthu ena a mu mdziko la Burkina Faso kuti achititse ma Demo akusakondwa pa zimene anayankhura President Traore kuti athetsa ulamuliro wa Democracy mdzikomo
Koma anthu aku Burkina Faso awauza azunguwo live live kuti βLeave us alone ife sitikuonapo Vuto tikazaona vuto mwina tizakuuzani koma padakalipano tili pambuyo pa President wathu Traore chifukwa chilichonse pano chikuyenda bwino ndiye musatuze zochitaβ