07/08/2024
poem : Tayimilira iwe Donah
ndik*t tayimilira iwe Donah
Mutsachere Bomba koma uchere nkhutu k*t
undivesese za kunkhosi kwanga ndikonyowa
Tayimilira iwe
panthawi imene tinakumana panali mphepo wa kavuluvulu koma chifkwa chak*t unakuwa "tikuferanji ife pano unatero " mmm pamenepo
mphepo inankhala bata
pamenepo mphepo imachita kuvomeleza chilengedwe chako achemwali
Tayimilira
Ndik*t tayimilira iwe Donah
ukamandiyona dzunguli dzunguli mpakwanu ngati khunda sichina ayi!! koma ndikulempera kugona chifukwa chak*t mbali inayi panthupi panga ndinaberedwa nthiti ku GENESIS nde ndkufuna ndibwerere nawo nthitiyo
tayimilira iwe
Tayimilira iwe Donah
chuluke chuluke wa njuchi unena yomwe wakuluma zonad akadzi nd maruwa koma maruwa akayombedwa ndizuwa wamafoto koma iwe ndiwe dzuwaro mmmm
chonde tayimilira iwe
Tayimilira iwe Donah
wazaza mtima mwanga ndasowa ponthawira
ndkuziwa k*t ndkankhala ndiwe ndasiya kulira
chonde ndichilitsen mabara wa mtima mwanga
ndilimbulanda ndi vekeni mmmm
kodi unalakwisa chan kwa Mulungu k*ti iwe ngero akugetsereni pasi panooo ? mamama
iwedi chisumphi anatayo nthawi polenga
Tayimilira iwe Donah
By ZYamikani Munthali
contact 0994884484
email [email protected]